Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:11 - Buku Lopatulika

Pomwepo Ayuda analikumfuna Iye pachikondwerero, nanena, Ali kuti uja?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pomwepo Ayuda analikumfuna Iye pachikondwerero, nanena, Ali kuti uja?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akulu a Ayuda ankamufunafuna kuchikondwereroko, nkumafunsana kuti, “Kodi amene uja ali kuti?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsopano kuphwandoko Ayuda anakamufunafuna ndi kumafunsana kuti, “Kodi munthu ameneyu ali kuti?”

Onani mutuwo



Yohane 7:11
6 Mawu Ofanana  

Ndipo umene ndiwo umboni wa Yohane, pamene Ayuda anatuma kwa iye ansembe ndi Alevi a ku Yerusalemu akamfunse iye, Ndiwe yani?


Pamenepo analikumfuna Yesu, nanena wina ndi mnzake poimirira iwo mu Kachisi, Muyesa bwanji inu, sadzadza kuchikondwerero kodi?


Ndipo zitapita izi Yesu anayendayenda mu Galileya; pakuti sanafune kuyendayenda mu Yudeya, chifukwa Ayuda anafuna kumupha Iye.


Chinkana anatero panalibe munthu analankhula za Iye poyera, chifukwa cha kuopa Ayuda.


Chifukwa chake Ayuda anazizwa, nanena, Ameneyu adziwa bwanji zolemba, wosaphunzira?


Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.