Yohane 7:13 - Buku Lopatulika13 Chinkana anatero panalibe munthu analankhula za Iye poyera, chifukwa cha kuopa Ayuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chinkana anatero panalibe munthu analankhula za Iye poyera, chifukwa cha kuopa Ayuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Komabe panalibe munthu wolankhula poyera za Iye, chifukwa choopa akulu a Ayuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Koma panalibe amene ankanena kalikonse poyera za Iye chifukwa choopa Ayuda. Onani mutuwo |