Yohane 7:14 - Buku Lopatulika14 Koma pamene padafika pakati pa chikondwerero, Yesu anakwera nalowa mu Kachisi, naphunzitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma pamene padafika pakati pa chikondwerero, Yesu anakwera nalowa m'Kachisi, naphunzitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Chikondwerero chija chikali pakati, Yesu adaloŵa m'Nyumba ya Mulungu nayamba kuphunzitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Phwando lili pakatikati, Yesu anapita ku bwalo la Nyumba ya Mulungu ndi kuyamba kuphunzitsa. Onani mutuwo |