Yohane 7:15 - Buku Lopatulika15 Chifukwa chake Ayuda anazizwa, nanena, Ameneyu adziwa bwanji zolemba, wosaphunzira? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Chifukwa chake Ayuda anazizwa, nanena, Ameneyu adziwa bwanji zolemba, wosaphunzira? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Akulu a Ayuda adadabwa nati, “Bwanji munthu ameneyu ali ndi nzeru zotere, pamene sadaphunzire konse?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ayuda anadabwa ndipo anafunsa kuti, “Kodi munthu uyu nzeru izi anazitenga kuti popanda kuphunzira?” Onani mutuwo |