Yohane 7:16 - Buku Lopatulika16 Pamenepo Yesu anayankha iwo, nati, Chiphunzitso changa sichili changa, koma cha Iye amene anandituma Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pamenepo Yesu anayankha iwo, nati, Chiphunzitso changa sichili changa, koma cha Iye amene anandituma Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Yesu adati, “Zimene ndimaphunzitsa si zangatu ai, ndi za Atate amene adandituma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yesu anayankha kuti, “Chiphunzitso changa si cha Ine ndekha. Chimachokera kwa Iye amene anandituma. Onani mutuwo |