Yohane 11:56 - Buku Lopatulika56 Pamenepo analikumfuna Yesu, nanena wina ndi mnzake poimirira iwo mu Kachisi, Muyesa bwanji inu, sadzadza kuchikondwerero kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201456 Pamenepo analikumfuna Yesu, nanena wina ndi mnzake poimirira iwo m'Kachisi, Muyesa bwanji inu, sadzadza kuchikondwerero kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa56 Ankamufunafuna Yesu, ndipo pamene adasonkhana m'Nyumba ya Mulungu ankafunsana kuti, “Kodi inu mukuganiza bwanji? Kodi monga Iye uja abwera kuchikondwerero kuno?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero56 Iwo anapitiriza kumufunafuna Yesu, ndipo pamene ankayimirira mʼbwalo la Nyumba ya Mulungu anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi ukuganiza chiyani? Kodi Iye sabwera konse kuphwando?” Onani mutuwo |