Yohane 11:55 - Buku Lopatulika55 Koma Paska wa Ayuda anali pafupi; ndipo ambiri anakwera kunka ku Yerusalemu kuchoka kuminda, asanafike Paska, kukadziyeretsa iwo okha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201455 Koma Paska wa Ayuda anali pafupi; ndipo ambiri anakwera kunka ku Yerusalemu kuchoka ku milaga, usanafike Paska, kukadziyeretsa iwo okha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa55 Chikondwerero cha Paska chija chinkayandikira. Choncho anthu ambiri ochokera ku midzi adapita ku Yerusalemu kukachita mwambo wa kudziyeretsa, Paska isanayambe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero55 Nthawi ya Paska wa Ayuda itayandikira, ambiri anakwera kupita ku Yerusalemu kuchokera ku madera a ku midzi chifukwa cha mwambo wa kuyeretsedwa Paska asanafike. Onani mutuwo |