Yohane 11:57 - Buku Lopatulika57 Koma ansembe aakulu ndi Afarisi adalamula kuti, munthu wina akadziwa pokhala Iye, aulule, kuti akamgwire Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201457 Koma ansembe aakulu ndi Afarisi adalamula kuti, munthu wina akadziwa pokhala Iye, aulule, kuti akamgwire Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa57 Koma akulu a ansembe ndi Afarisi anali atalamula kuti aliyense akadziŵa kumene kuli Yesu, aŵadziŵitse, kuti akamgwire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero57 Koma akulu a ansembe ndi Afarisi anapereka lamulo kuti ngati wina aliyense adziwe kumene kunali Yesu, iye akawawuze kuti akamugwire. Onani mutuwo |