Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 9:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Anthuwo adamufunsa kuti, “Iyeyo ali kuti?” Munthu uja adati, “Kaya, sindikudziŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Iwo anamufunsa iye kuti, “Ali kuti munthu ameneyu?” Iye anati, “Ine sindikudziwa.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:12
5 Mawu Ofanana  

Pomwepo Ayuda analikumfuna Iye pachikondwerero, nanena, Ali kuti uja?


Iyeyu anayankha, Munthuyo wotchedwa Yesu anakanda thope, napaka m'maso mwanga, nati, kwa ine, Muka ku Siloamu kasambe; chifukwa chake ndinachoka, ndipo m'mene ndinasamba ndinapenya.


Anapita naye amene anali wosaona kale kwa Afarisi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa