Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 9:11 - Buku Lopatulika

11 Iyeyu anayankha, Munthuyo wotchedwa Yesu anakanda thope, napaka m'maso mwanga, nati, kwa ine, Muka ku Siloamu kasambe; chifukwa chake ndinachoka, ndipo m'mene ndinasamba ndinapenya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Iyeyu anayankha, Munthuyo wotchedwa Yesu anakanda thope, napaka m'maso mwanga, nati, kwa ine, Muka ku Siloamu kasambe; chifukwa chake ndinachoka, ndipo m'mene ndinasamba ndinapenya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Iyeyo adati, “Munthu uja amati Yesuyu anakanda thope nalipaka m'maso mwangamu. Kenaka anandiwuza kuti, ‘Pita, ukasambe ku Siloamu. Ndinapitadi, ndipo nditasamba, ndayamba kupenya.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Iye anayankha kuti, “Munthu wina wotchedwa Yesu anakanda dothi ndi kupaka mʼmaso anga. Iye anandiwuza kuti ndipite ku Siloamu ndi kukasamba. Choncho ndinapita kukasamba, ndipo ndikuona.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:11
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anamfunsa Baruki, kuti, Utifotokozeretu, Unalemba bwanji mau awa onse ponena iye?


Kapena iwo aja khumi ndi asanu ndi atatu, amene nsanja yaitali ya mu Siloamu inawagwera, ndi kuwapha; kodi muyesa kuti iwo anali olakwa koposa anthu onse akukhala m'Yerusalemu?


Pamenepo anenana ndi iye, Nanga maso ako anatseguka bwanji?


Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.


Iye anayankha iwo, Ndinakuuzani kale, ndipo simunamve; mufuna kumvanso bwanji? Kodi inunso mufuna kukhala ophunzira ake?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa