Yohane 9:10 - Buku Lopatulika10 Pamenepo anenana ndi iye, Nanga maso ako anatseguka bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pamenepo anenana ndi iye, Nanga maso ako anatseguka bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Apo anthu aja adamufunsa kuti, “Nanga maso ako apenya bwanji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iwo anafunsitsa kuti, “Kodi nanga maso ako anatsekuka bwanji?” Onani mutuwo |