Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 2:3 - Buku Lopatulika

Ndipo pakutha vinyo, amake wa Yesu ananena naye, Alibe vinyo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pakutha vinyo, amake wa Yesu ananena naye, Alibe vinyo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene vinyo adatha, amai ake a Yesu adamuuza kuti, “Waŵathera vinyo.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Vinyo atatha, amayi a Yesu anati kwa Iye, “Wawathera vinyo.”

Onani mutuwo



Yohane 2:3
8 Mawu Ofanana  

ndi vinyo wokondweretsa mtima wa munthu, ndi mafuta akunyezimiritsa nkhope yake, ndi mkate wakulimbitsa mtima wa munthu.


Amaphikira zakudya kuti asekere, vinyo nakondweretsa moyo; ndipo ndalama zivomera zonse.


Muli mfuu m'makwalala chifukwa cha vinyo; kukondwa konse kwadetsedwa, kusangalala kwa dziko kwatha.


pakuti ichi ndi mwazi wanga wa pangano wothiridwa chifukwa cha anthu ambiri ku kuchotsa machimo.


Pamenepo alongo ake anatumiza kwa Iye, nanena, Ambuye, onani, amene mumkonda adwala.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.


Musadere nkhawa konse; komatu m'zonse ndi pemphero, ndi pembedzero, pamodzi ndi chiyamiko, zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu.