Masalimo 104:15 - Buku Lopatulika15 ndi vinyo wokondweretsa mtima wa munthu, ndi mafuta akunyezimiritsa nkhope yake, ndi mkate wakulimbitsa mtima wa munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 ndi vinyo wokondweretsa mtima wa munthu, ndi mafuta akunyezimiritsa nkhope yake, ndi mkate wakulimbitsa mtima wa munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Amapezamo vinyo wosangalatsa mtima wake, mafuta odzola kuti thupi lake lisisire, ndiponso buledi kuti ampatse mphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 vinyo amene amasangalatsa mtima wa munthu, mafuta amene amachititsa nkhope yake kuwala, ndi buledi amene amapereka mphamvu. Onani mutuwo |