Mateyu 26:28 - Buku Lopatulika28 pakuti ichi ndi mwazi wanga wa pangano wothiridwa chifukwa cha anthu ambiri ku kuchotsa machimo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 pakuti ichi ndi mwazi wanga wa pangano wothiridwa chifukwa cha anthu ambiri ku kuchotsa machimo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Pakuti aŵa ndi magazi anga otsimikiza Chipangano cha Mulungu. Magazi ameneŵa ndiŵakhetsa chifukwa cha anthu ochuluka, kuti Mulungu aŵakhululukire machimo ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Awa ndi magazi anga a pangano amene akhetsedwa chifukwa cha ambiri kuti akhululukidwe machimo. Onani mutuwo |