Mateyu 26:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo pamene anatenga chikho, anayamika, napatsa iwo, nanena, Mumwere ichi inu nonse, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo pamene anatenga chikho, anayamika, napatsa iwo, nanena, Mumwere ichi inu nonse, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Kenaka adatenga chikho, nathokoza Mulungu nkuchipereka kwa ophunzirawo. Adaŵauza kuti, “Imwani nonsenu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Kenaka anatenga chikho, nayamika nachipereka kwa iwo nati, “Imwani nonsenu. Onani mutuwo |