Mlaliki 10:19 - Buku Lopatulika19 Amaphikira zakudya kuti asekere, vinyo nakondweretsa moyo; ndipo ndalama zivomera zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Amaphikira zakudya kuti asekere, vinyo nakondweretsa moyo; ndipo ndalama zivomera zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Phwando ndi lokondwetsa anthu, ndipo vinyo ndi wosangalatsa moyo. Komatu zonsezo nzolira ndalama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Phwando ndi lokondweretsa anthu, ndipo vinyo ndi wosangalatsa moyo, koma ndalama ndi yankho la chilichonse. Onani mutuwo |