Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 2:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Vinyo atatha, amayi a Yesu anati kwa Iye, “Wawathera vinyo.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Ndipo pakutha vinyo, amake wa Yesu ananena naye, Alibe vinyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo pakutha vinyo, amake wa Yesu ananena naye, Alibe vinyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Pamene vinyo adatha, amai ake a Yesu adamuuza kuti, “Waŵathera vinyo.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 2:3
8 Mawu Ofanana  

vinyo amene amasangalatsa mtima wa munthu, mafuta amene amachititsa nkhope yake kuwala, ndi buledi amene amapereka mphamvu.


Phwando ndi lokondweretsa anthu, ndipo vinyo ndi wosangalatsa moyo, koma ndalama ndi yankho la chilichonse.


Anthu akulira mʼmisewu kufuna vinyo; chimwemwe chonse chatheratu, palibenso chisangalalo pa dziko lapansi.


Awa ndi magazi anga a pangano amene akhetsedwa chifukwa cha ambiri kuti akhululukidwe machimo.


Choncho alongo ake anatumiza mawu kwa Yesu kuti, “Ambuye, uja amene Inu mumamukonda akudwala.”


ndipo Yesu ndi ophunzira ake anayitanidwanso ku ukwatiwo.


Yesu anayankha kuti, “Amayi, chifukwa chiyani mukundiwuza Ine? Nthawi yanga sinakwane.”


Musade nkhawa ndi kanthu kalikonse, koma pa china chilichonse, mwa pemphero ndi chidandaulo pamodzi ndi chiyamiko, perekani zopempha zanu kwa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa