Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 2:29 - Buku Lopatulika

Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono pabwere fuko la Nafutali, limene mtsogoleri wake ndi Ahira mwana wa Enani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Lotsatira lidzakhala fuko la Nafutali. Mtsogoleri wa Anafutali ndi Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo



Numeri 2:29
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Rakele anati, Ndi malimbano a Mulungu ndalimbana naye mkulu wanga, ndipo ndapambana naye; ndipo anamutcha dzina lake Nafutali.


Wa Nafutali, Ahira mwana wa Enani.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Nafutali anayang'anira Ahira mwana wa Enani.


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu chimodzi kudza mazana asanu.


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.


Tsiku lakhumi ndi chiwiri kalonga wa ana a Nafutali, ndiye Ahira mwana wa Enani:


ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ichi ndi chopereka cha Ahira mwana wa Enani.