Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:83 - Buku Lopatulika

83 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ichi ndi chopereka cha Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

83 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ichi ndi chopereka cha Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

83 Ndipo zoperekera nsembe yachiyanjano zinali ng'ombe ziŵiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, ndi anaankhosa asanu amphongo a chaka chimodzi. Zimenezi ndizo zinali zopereka za Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

83 ngʼombe zazimuna ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu, ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:83
4 Mawu Ofanana  

Wa Nafutali, Ahira mwana wa Enani.


Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani.


tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;


Uku ndi kupereka chiperekere guwa la nsembe, ndi akalonga a Israele, tsiku la kudzoza kwake: mbale zasiliva khumi ndi ziwiri, mbale zowazira zasiliva khumi ndi ziwiri, zipande zagolide khumi ndi ziwiri;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa