Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 10:27 - Buku Lopatulika

27 Ndi pa gulu la fuko la ana a Nafutali anayang'anira Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndi pa gulu la fuko la ana a Nafutali anayang'anira Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Mtsogoleri wa gulu la fuko la Nafutali anali Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 ndipo mtsogoleri wa mtundu wa Nafutali anali Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:27
4 Mawu Ofanana  

Wa Nafutali, Ahira mwana wa Enani.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Asere anayang'anira Pagiyele mwana wa Okarani.


Potero maulendo a ana a Israele anakhala monga mwa magulu ao; nayenda ulendo wao.


Tsiku lakhumi ndi chiwiri kalonga wa ana a Nafutali, ndiye Ahira mwana wa Enani:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa