Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 17:12 - Buku Lopatulika

Pamenepo ana a Israele ananena ndi Mose, nati, Taonani, tikufa, tionongeka, tionongeka tonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo ana a Israele ananena ndi Mose, nati, Taonani, tikufa, tionongeka, tionongeka tonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Aisraele adauza Mose kuti, “Tatayika, tonsefe taferatu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aisraeli anati kwa Mose, “Tikufa! Tatayika, tonse tatayika!

Onani mutuwo



Numeri 17:12
8 Mawu Ofanana  

Pakuti tionongeka mu mkwiyo wanu; ndipo m'kuzaza kwanu tiopsedwa.


Utsiru wa munthu ukhotetsa njira yake; mtima wake udandaula pa Yehova.


Pakuti sindidzatsutsana kunthawi zonse, sindidzakwiya masiku onse; pakuti mzimu udzalefuka pamaso pa Ine, ndi miyoyo imene ndinailenga.


Ndipo ine ndinati, Tsoka kwa ine! Chifukwa ndathedwa; chifukwa ndili munthu wa milomo yonyansa, ndikhala pakati pa anthu a milomo yonyansa; chifukwa kuti maso anga aona Mfumu, Yehova wa makamu.


Ndipo Mose anachita monga Yehova adamuuza, momwemo anachita.


ndipo lidzakhala kwa iye, ndi kwa mbeu zake zakumtsata pangano la unsembe wosatha, popeza anachita nsanje chifukwa cha Mulungu wake, anawachitira ana a Israele chowatetezera.


Koma sanafe ana aamuna a Kora.


ndipo mwaiwala dandauliro limene linena nanu monga ndi ana, Mwana wanga, usayese chopepuka kulanga kwa Ambuye, kapena usakomoke podzudzulidwa ndi Iye;