Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 17:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Aisraeli anati kwa Mose, “Tikufa! Tatayika, tonse tatayika!

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

12 Pamenepo ana a Israele ananena ndi Mose, nati, Taonani, tikufa, tionongeka, tionongeka tonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Pamenepo ana a Israele ananena ndi Mose, nati, Taonani, tikufa, tionongeka, tionongeka tonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Tsono Aisraele adauza Mose kuti, “Tatayika, tonsefe taferatu.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 17:12
8 Mawu Ofanana  

Ife tathedwa ndi mkwiyo wanu; ndipo taopsezedwa ndi kuyipidwa kwanu.


Uchitsiru wa munthu umamubweretsera zovuta, mtima wake umakwiyira Yehova.


Sindidzawatsutsa anthu mpaka muyaya kapena kuwapsera mtima nthawi zonse, popeza kuti ndinalenga anthu anga ndi kuwapatsa mpweya wamoyo.


Tsono ine ndinafuwula kuti, “Tsoka langa ine! Ndatayika! Pakuti ndine munthu wapakamwa poyipa, ndipo ndimakhala pakati pa anthu a pakamwa poyipa, ndipo ndi maso anga ndaona mfumu Yehova Wamphamvuzonse.”


Mose anachita monga Yehova anamulamulira.


Ndikupangana naye pangano la unsembe wosatha, iyeyo pamodzi ndi zidzukulu zake zonse, chifukwa sanalole kuti anthu awukire Ine Mulungu, ndipo anachita ntchito yopepesera machimo Aisraeli.”


Koma ana a Kora sanafe nawo.


Kodi mwayiwala mawu olimbitsa mtima aja, amene Mulungu anayankhula kwa inu ngati ana ake? Mawuwo ndi awa: “Mwana wanga, usapeputse kulanga kwa Ambuye ndipo usataye mtima pamene akukudzudzula.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa