Numeri 25:13 - Buku Lopatulika13 ndipo lidzakhala kwa iye, ndi kwa mbeu zake zakumtsata pangano la unsembe wosatha, popeza anachita nsanje chifukwa cha Mulungu wake, anawachitira ana a Israele chowatetezera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 ndipo lidzakhala kwa iye, ndi kwa mbeu zake zakumtsata pangano la unsembe wosatha, popeza anachita nsanje chifukwa cha Mulungu wake, anawachitira ana a Israele chowatetezera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndikupangana naye iyeyu ndi zidzukulu zake zonse, chipangano cha unsembe wamuyaya, chifukwa sadalole kuti anthu aukire Ine Mulungu, ndipo adachita ntchito yopepesera machimo a Aisraele.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndikupangana naye pangano la unsembe wosatha, iyeyo pamodzi ndi zidzukulu zake zonse, chifukwa sanalole kuti anthu awukire Ine Mulungu, ndipo anachita ntchito yopepesera machimo Aisraeli.” Onani mutuwo |