Numeri 25:14 - Buku Lopatulika14 Koma dzina la Mwisraele adamuphayo, ndiye amene adamupha pamodzi ndi mkazi Mmidiyani, ndiye Zimiri mwana wa Salu, mfumu ya nyumba ya makolo mwa Asimeoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma dzina la Mwisraele adamuphayo, ndiye amene adamupha pamodzi ndi mkazi Mmidiyani, ndiye Zimiri mwana wa Salu, mfumu ya nyumba ya makolo mwa Asimeoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Mwisraele amene adaphedwa pamodzi ndi mkazi Wachimidiyani uja anali Zimiri mwana wa Salu, mtsogoleri wa banja la makolo a Asimeoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Dzina la Mwisraeli yemwe anaphedwa ndi mkazi wa Chimidiyani anali Zimuri mwana wa Salu, mtsogoleri wa banja la Simeoni. Onani mutuwo |