Numeri 25:15 - Buku Lopatulika15 Ndi dzina la mkazi Mmidiyani adamuphayo ndiye Kozibi mwana wamkazi wa Zuri; ndiye mkulu wa anthu a nyumba ya makolo mu Midiyani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndi dzina la mkazi Mmidiyani adamuphayo ndiye Kozibi mwana wamkazi wa Zuri; ndiye mkulu wa anthu a nyumba ya makolo m'Midiyani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndipo mkazi Wachimidiyani amene adaphedwayo anali Kozibi mwana wa Zuri, amene anali mtsogoleri wa mbumba ina ya fuko la ku Midiyani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndipo dzina la mkazi wa Chimidiyani, yemwe anaphedwayo, linali Kozibi mwana wa Zuri, mtsogoleri wa fuko la ku Midiyaniko. Onani mutuwo |