Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 17:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo Mose anachita monga Yehova adamuuza, momwemo anachita.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo Mose anachita monga Yehova adamuuza, momwemo anachita.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Mose adachita momwemo. Adatsatadi zomwe Chauta adalamula.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Mose anachita monga Yehova anamulamulira.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 17:11
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ukakudzerani mlandu uliwonse wochokera kwa abale anu okhala m'mizinda mwao, kusiyanitsa pakati pa mwazi ndi mwazi, pakati pa chilamulo ndi chiuzo, malemba ndi maweruzo, muwachenjeze kuti asapalamule kwa Yehova, angafikitsire inu nokha ndi abale anu mkwiyo; muzitero, ndipo simudzapalamula.


Pamenepo aiphe mbuzi ya nsembe yauchimo, ndiyo yophera anthu, nalowe nao mwazi wake m'tseri mwa nsalu yotchinga, nachite nao mwazi wake monga umo anachitira ndi mwazi wa ng'ombe, nauwaze pachotetezerapo ndi chakuno cha chotetezerapo;


nachitire chotetezera malo opatulika, chifukwa cha kudetsedwa kwa ana a Israele, ndi chifukwa cha zolakwa zao, monga mwa zochimwa zao zonse; nachitire chihema chokomanako momwemo, chakukhala nao pakati pa zodetsa zao.


Nyamayi ikali pakati pa mano, asanaitafune, Mulungu anapsa mtima pa anthuwa, ndipo Yehova anawakantha anthu ndi kukantha kwakukulu ndithu.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Bweza ndodo ya Aroni kuiika chakuno cha mboni, isungike ikhale chizindikiro cha pa ana opikisana; kuti unditsirizire madandaulo ao, kuti ungafe.


Pamenepo ana a Israele ananena ndi Mose, nati, Taonani, tikufa, tionongeka, tionongeka tonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa