Masalimo 90:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti tionongeka mu mkwiyo wanu; ndipo m'kuzaza kwanu tiopsedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti tionongeka mu mkwiyo wanu; ndipo m'kuzaza kwanu tiopsedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ife tapseratu ndi mkwiyo wanu woyaka, tikufa ndi mantha chifukwa cha ukali wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ife tathedwa ndi mkwiyo wanu; ndipo taopsezedwa ndi kuyipidwa kwanu. Onani mutuwo |