Masalimo 90:6 - Buku Lopatulika6 Mamawa uphuka bwino; madzulo ausenga, nuuma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Mamawa uphuka bwino; madzulo ausenga, nuuma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 M'mamaŵamo umatsitsimuka ndipo umakondwa. Madzulo umafota ndi kuuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 ngakhale kuti mmawa umaphuka watsopano, pofika madzulo wauma ndi kufota. Onani mutuwo |