Masalimo 90:5 - Buku Lopatulika5 Muwatenga ngati ndi madzi aakulu, akhala ngati tulo; mamawa akhala ngati msipu wophuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Muwatenga ngati ndi madzi aakulu, akhala ngati tulo; mamawa akhala ngati msipu wophuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Inu mumachotsa moyo wa anthu mwadzidzidzi. Ali ngati maloto, ali ngati udzu wongotsitsimuka m'maŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Inu mumasesa anthu mʼtulo ta imfa, iwo ali ngati udzu watsopano wa mmawa, Onani mutuwo |