Masalimo 90:8 - Buku Lopatulika8 Munaika mphulupulu zathu pamaso panu, ndi zoipa zathu zobisika pounikira nkhope yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Munaika mphulupulu zathu pamaso panu, ndi zoipa zathu zobisika pounikira nkhope yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inu mwaika machimo athu pamaso panu, ngakhale machimo obisika mwaŵaonetsa poyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mwayika mphulupulu zathu pamaso panu, machimo athu obisika poonekera pamaso panu. Onani mutuwo |