Masalimo 90:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti masiku athu onse apitirira mu ukali wanu; titsiriza moyo wathu ngati lingaliro. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti masiku athu onse apitirira m'ukali wanu; titsiriza moyo wathu ngati lingaliro. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pajatu masiku athu amachepa chifukwa cha mkwiyo wanu, zaka zathu zimatha ngati kuusa moyo chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Masiku athu onse amatha ali pansi pa ukali wanu; timatsiriza zaka zathu ndi kubuwula. Onani mutuwo |