Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 16:49 - Buku Lopatulika

Koma akufa nao mliri ndiwo zikwi khumi ndi zinai mphambu mazana asanu ndi awiri, osawerenga aja adafera chija cha Kora.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma akufa nao mliri ndiwo zikwi khumi ndi zinai mphambu mazana asanu ndi awiri, osawerenga aja adafera chija cha Kora.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komabe amene adafa ndi mliriwo anali 14,700, kuwonjeza pa anthu aja amene adafa pa mlandu wa Kora.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Komabe anthu 14, 700 anafa ndi mliriwo, kuwonjezera pa aja amene anafa chifukwa cha Kora.

Onani mutuwo



Numeri 16:49
10 Mawu Ofanana  

Momwemo Yehova anatumiza mliri pa Israele; ndipo adagwapo amuna zikwi makumi asanu ndi awiri a Israele.


amuna amene anaipsa mbiri ya dziko, anafa ndi mliri pamaso pa Yehova.


Ndipo anaima pakati pa akufa ndi amoyo; ndi mliri unaleka.


Ndipo Aroni anabwera kwa Mose ku khomo la chihema chokomanako; ndi mliri unaleka.


Ndipo akufa nao mliri ndiwo zikwi makumi awiri ndi zinai.


Kapena musadandaula, monga ena a iwo anadandaula, naonongeka ndi woonongayo.


Penyani musakane wolankhulayo. Pakuti ngati iwowa sanapulumuke, pomkana Iye amene anawachenjeza padziko, koposatu sitidzapulumuka ife, odzipatulira kwa Iye wa Kumwamba;