Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 16:50 - Buku Lopatulika

50 Ndipo Aroni anabwera kwa Mose ku khomo la chihema chokomanako; ndi mliri unaleka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

50 Ndipo Aroni anabwera kwa Mose ku khomo la chihema chokomanako; ndi mliri unaleka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

50 Pambuyo pake Aroni adabwerera kwa Mose ku chipata cha chihema chamsonkhano, mliriwo utaleka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

50 Ndipo Aaroni anabwerera kwa Mose ku khomo la tenti ya msonkhano, chifukwa mliriwo unali utatha.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 16:50
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose ndi Aroni anadza kukhomo kwa chihema chokomanako.


Koma akufa nao mliri ndiwo zikwi khumi ndi zinai mphambu mazana asanu ndi awiri, osawerenga aja adafera chija cha Kora.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa