1 Akorinto 10:10 - Buku Lopatulika10 Kapena musadandaula, monga ena a iwo anadandaula, naonongeka ndi woonongayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Kapena musadandaula, monga ena a iwo anadandaula, naonongeka ndi woonongayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Musadandaule monga momwe adaadandaulira ena mwa iwo: paja adaphedwa ndi mngelo wodzetsa imfa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo osamawiringula, monga ena mwa iwo anachitira naphedwa ndi mngelo wowononga. Onani mutuwo |