Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 10:9 - Buku Lopatulika

9 Kapena tisayese Ambuye, monga ena a iwo anayesa, naonongeka ndi njoka zija.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Kapena tisayese Ambuye, monga ena a iwo anayesa, naonongeka ndi njoka zija.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Tisapute Ambuye monga momwe adaaŵaputira ena mwa iwo: paja anthuwo adaphedwa ndi njoka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Tisamuyese Khristu, monga ena mwa iwo anachitira ndipo anaphedwa ndi njoka.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 10:9
11 Mawu Ofanana  

Popeza analakalakatu kuchidikhako, nayesa Mulungu m'chipululu.


Ndipo anayesa Mulungu mumtima mwao ndi kupempha chakudya monga mwa kulakalaka kwao.


Koma anamuyesa napikisana ndi Mulungu Wam'mwambamwamba, osasunga mboni zake;


Pamene makolo anu anandisuntha, anandiyesa, anapenyanso chochita Ine.


Pamenepo anthu anatsutsana ndi Mose, nati, Tipatseni madzi timwe. Koma Mose ananena nao, Mutsutsana nane bwanji? Muyeseranji Yehova?


Ndipo anatcha dzina la malowo Masa, ndi Meriba, chifukwa cha kutsutsana kwa ana a Israele; popezanso anayesa Yehova, ndi kuti, Kodi Yehova ali pakati pa ife, kapena iai?


Musamayesa Yehova Mulungu wanu, monga munamyesa mu Masa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa