1 Akorinto 10:9 - Buku Lopatulika9 Kapena tisayese Ambuye, monga ena a iwo anayesa, naonongeka ndi njoka zija. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Kapena tisayese Ambuye, monga ena a iwo anayesa, naonongeka ndi njoka zija. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tisapute Ambuye monga momwe adaaŵaputira ena mwa iwo: paja anthuwo adaphedwa ndi njoka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Tisamuyese Khristu, monga ena mwa iwo anachitira ndipo anaphedwa ndi njoka. Onani mutuwo |