Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 15:34 - Buku Lopatulika

Ndipo anayamba wamsunga, popeza sichinanenedwe choyenera kumchitira iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anathanga wamsunga, popeza sichinanenedwa choyenera kumchitira iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwo adamponya m'ndende chifukwa choti sankadziŵa bwino zoti amchite.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo anamutsekera mʼndende chifukwa sankadziwa choti achite naye.

Onani mutuwo



Numeri 15:34
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene mpongozi wake wa Mose anaona zonsezi iye anawachitira anthu, anati, Chinthu ichi nchiyani uwachitira anthuchi? Umakhala pa wekha bwanji, ndi anthu onse amakhala chilili pamaso pako kuyambira m'mawa kufikira madzulo?


Ndipo Mose anati kwa mpongozi wake, Chifukwa anthu amadza kwa ine kudzafunsira Mulungu;


Ndipo anamsunga m'kaidi, kuti awafotokozere m'mene anenere Yehova.


Ndipo amene adampezawo alinkufuna nkhuni anabwera naye kwa Mose ndi Aroni, ndi kwa khamu lonse.


Ndipo Mose ananena nao, Baimani; ndimve chouza Yehova za inu.