Eksodo 18:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Mose anati kwa mpongozi wake, Chifukwa anthu amadza kwa ine kudzafunsira Mulungu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Mose anati kwa mpongozi wake, Chifukwa anthu amadza kwa ine kudzafunsira Mulungu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mose adayankha kuti, “Ndiyenera kuchita zimenezi chifukwa choti anthu amabwera kwa ine, kuti amve zimene Mulungu afuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mose anamuyankha kuti, “Chifukwa anthuwa anabwera kwa ine kudzafunsa zimene Mulungu akufuna. Onani mutuwo |