Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 15:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo amene adampezawo alinkufuna nkhuni anabwera naye kwa Mose ndi Aroni, ndi kwa khamu lonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo amene adampezawo alinkufuna nkhuni anabwera naye kwa Mose ndi Aroni, ndi kwa khamu lonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Amene adapeza munthuyo akutola nkhuni, adabwera naye kwa Mose ndi Aroni ndi kwa mpingo wonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Amene anamupeza akutola nkhunizo anabwera naye kwa Mose ndi Aaroni ndi kwa gulu lonse

Onani mutuwo Koperani




Numeri 15:33
4 Mawu Ofanana  

ndipo iwo aweruze milandu ya anthu nthawi zonse; ndipo kudzakhala kuti milandu yaikulu yonse abwere nayo kwa iwe; koma milandu yaing'ono yonse aweruze okha; potero idzakuchepera ntchito, ndi iwo adzasenza nawe.


Ndipo pokhala ana a Israele m'chipululu, anapeza munthu wakufuna nkhuni tsiku la Sabata.


Ndipo anayamba wamsunga, popeza sichinanenedwe choyenera kumchitira iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa