Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 24:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo anamsunga m'kaidi, kuti awafotokozere m'mene anenere Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo anamsunga m'kaidi, kuti awafotokozere m'mene anenere Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Adamuika m'ndende mpaka atadziŵa kufuna kwa Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Anamuyika mʼndende mpaka atadziwa bwino chofuna cha Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 24:12
7 Mawu Ofanana  

Ukachite chinthuchi, ndi Mulungu akakuuza chotero, udzakhoza kupirira, ndi anthu awa onse adzapita kwao mumtendere.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Ndipo anayamba wamsunga, popeza sichinanenedwe choyenera kumchitira iye.


Ndipo Mose anapita nao mlandu wao pamaso pa Yehova.


Ndipo Mose ananena nao, Baimani; ndimve chouza Yehova za inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa