Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 15:22 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene mulakwa, osachita mau awa onse amene Yehova ananena ndi Mose;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene mulakwa, osachita mau awa onse amene Yehova ananena ndi Mose;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Koma mwina mutha kulakwa mosadziŵa, osasunga malamulo onse amene Chauta adauza Mose,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“ ‘Ndipo ngati muchimwa mosadziwa posasunga ena mwa malamulo awa amene Yehova wapereka kwa Mose,

Onani mutuwo



Numeri 15:22
10 Mawu Ofanana  

Adziwitsa zolowereza zake ndani? Mundimasule kwa zolakwa zobisika.


Lankhula ndi ana a Israele, ndi kuti, Munthu akachimwa, osati dala, pa china cha zinthu zilizonse aziletsa Yehova, nakachitapo kanthu;


Akachimwa mkulu, osati dala, pa china cha zinthu zilizonse aziletsa Yehova Mulungu wake, napalamula;


Ndipo akachimwa wina wa anthu a m'dziko, osati dala, pa china cha zinthu zilizonse aziletsa Yehova, napalamula;


Ndipo wansembe amchitire chomtetezera chifukwa cha kuchimwa kwake adachimwira chimodzi cha izi, ndipo adzakhululukidwa; ndipo chotsalira chikhale cha wansembe, monga umo amachitira chopereka chaufacho.


Muzipatsa Yehova nsembe yokweza yoitenga ku mtanda wanu woyamba, mwa mibadwo yanu.


ndizo zonse Yehova anakuuzani ndi dzanja la Mose, kuyambira tsikulo Yehova analamula, ndi kunkabe m'mibadwo yanu;


Koma iye amene sanachidziwe, ndipo anazichita zoyenera mikwapulo, adzakwapulidwa pang'ono. Ndipo kwa munthu aliyense adampatsa zambiri, kwa iye adzafuna zambiri; ndipo amene anamuikizira zambiri, adzamuuza abwezere zoposa.