Levitiko 4:22 - Buku Lopatulika22 Akachimwa mkulu, osati dala, pa china cha zinthu zilizonse aziletsa Yehova Mulungu wake, napalamula; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Akachimwa mkulu, osati dala, pa china cha zinthu zilizonse aziletsa Yehova Mulungu wake, napalamula; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 “Wolamula akachimwa mosadziŵa, kuchimwira Chauta, Mulungu wake, pa chinthu choletsedwa, napalamula pakutero, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 “ ‘Ngati mtsogoleri achimwa mosadziwa nachita zimene ndi zoletsedwa ndi Yehova Mulungu wake, ndiye kuti wapalamula. Onani mutuwo |