Levitiko 4:2 - Buku Lopatulika2 Lankhula ndi ana a Israele, ndi kuti, Munthu akachimwa, osati dala, pa china cha zinthu zilizonse aziletsa Yehova, nakachitapo kanthu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Lankhula ndi ana a Israele, ndi kuti, Munthu akachimwa, osati dala, pa china cha zinthu zilizonse aziletsa Yehova, nakachitapo kanthu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Uza Aisraele kuti pa zonse zimene Chauta adaletsa, munthu aliyense akachimwapo mosadziŵa, pochita kanthu kena kalikonse koletsedwa, azichita izi: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Awuze Aisraeli kuti, ‘Munthu akachimwa mosadziwa ndi kuchita chilichonse chimene Yehova walamula kuti asachite, azichita izi: Onani mutuwo |