Numeri 15:21 - Buku Lopatulika21 Muzipatsa Yehova nsembe yokweza yoitenga ku mtanda wanu woyamba, mwa mibadwo yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Muzipatsa Yehova nsembe yokweza yoitenga ku mtanda wanu woyamba, mwa mibadwo yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Muzidzapereka motero kwa Chauta buledi mmodzi mwa buledi wanu woyamba pa mibadwo yanu yonse.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pa mibado yanu yonse muzidzapereka chopereka ichi kwa Yehova kuchokera ku zakudya zanu zoyamba za mʼnthaka. Onani mutuwo |