Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 15:23 - Buku Lopatulika

23 ndizo zonse Yehova anakuuzani ndi dzanja la Mose, kuyambira tsikulo Yehova analamula, ndi kunkabe m'mibadwo yanu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 ndizo zonse Yehova anakuuzani ndi dzanja la Mose, kuyambira tsikulo Yehova anauza, ndi kunkabe m'mibadwo yanu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 ndi zonse zimene adakulamulani kudzera mwa Mose, kuyambira tsiku limene Chauta adapereka lamulo mpaka m'tsogolo mwake pa mibadwo yanu yonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 lina lililonse mwa malamulo a Yehova amene wapereka kwa inu kudzera mwa Mose, kuyambira tsiku limene Yehova anawapereka mpaka mibado ya mʼtsogolo,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 15:23
2 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene mulakwa, osachita mau awa onse amene Yehova ananena ndi Mose;


pamenepo kudzali, ngati anachichita osati dala, osachidziwa khamulo, khamu lonse lipereke ng'ombe yamphongo ikhale nsembe yopsereza, ya fungo lokoma ya Yehova, pamodzi ndi nsembe yake yaufa, ndi nsembe yake yothira, monga mwa chiweruzo chake; ndi tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa