Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 12:12 - Buku Lopatulika

Asakhaletu iye ngati wakufa, amene dera lina la mnofu wake watha potuluka iye m'mimba mwa make.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Asakhaletu iye ngati wakufa, amene dera lina la mnofu wake watha potuluka iye m'mimba mwa make.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Musalole kuti Miriyamu akhale ngati mwana wobadwa wakufa, amene thupi lake lili loonongeka kumodzi.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Musalole kuti Miriamu akhale ngati mwana wobadwa wakufa kuchoka mʼmimba mwa amayi ake, thupi lake litawonongeka.”

Onani mutuwo



Numeri 12:12
9 Mawu Ofanana  

Kapena ngati nsenye yobisika ndikadakhala kuli zii; ngati makanda osaona kuunika.


Apite ngati nkhono yosungunuka; asaone dzuwa monga mtayo.


Ndipo Aroni anati kwa Mose, Mfumu yanga, musatiikiretu kuchimwa kumene tapusa nako, ndi kuchimwa nako.


Ndipo Mose anafuulira kwa Yehova, ndi kuti, Mchiritsenitu, Mulungu.


ndipo potsiriza pake pa onse, anaoneka kwa inenso monga mtayo.


Ndipo inu, pokhala akufa m'zolakwa ndi kusadulidwa kwa thupi lanu, anakupatsani moyo pamodzi ndi Iye, m'mene adatikhululukira ife zolakwa zonse;


Koma iye wakutsata zomkondweretsa, adafa pokhala ali ndi moyo.