1 Timoteyo 5:6 - Buku Lopatulika6 Koma iye wakutsata zomkondweretsa, adafa pokhala ali ndi moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma iye wakutsata zomkondweretsa, adafa pokhala ali ndi moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma mai wamasiye amene amangodzisangalatsa ndi zapansipano, ameneyo wafa kale ngakhale akali moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma mkazi wamasiye amene amangokhalira kuchita zosangalatsa moyo wake, wafa kale ngakhale akanali ndi moyo. Onani mutuwo |