Numeri 12:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Musalole kuti Miriamu akhale ngati mwana wobadwa wakufa kuchoka mʼmimba mwa amayi ake, thupi lake litawonongeka.” Onani mutuwoBuku Lopatulika12 Asakhaletu iye ngati wakufa, amene dera lina la mnofu wake watha potuluka iye m'mimba mwa make. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Asakhaletu iye ngati wakufa, amene dera lina la mnofu wake watha potuluka iye m'mimba mwa make. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Musalole kuti Miriyamu akhale ngati mwana wobadwa wakufa, amene thupi lake lili loonongeka kumodzi.” Onani mutuwo |