Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 58:8 - Buku Lopatulika

8 Apite ngati nkhono yosungunuka; asaone dzuwa monga mtayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Apite ngati nkhono yosungunuka; asaone dzuwa monga mtayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Akhale ngati nkhonodambe imene imazimirira poyenda, ngati mtayo wosaona dzuŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Akhale ngati nkhono imene imasungunuka pamene ikuyenda; ngati mwana wakufa asanabadwe, iwo asaone dzuwa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 58:8
6 Mawu Ofanana  

Ndikadakhala monga ngati sindikadakhala; akadanditenga pobadwapo kunka nane kumanda.


Kapena ngati nsenye yobisika ndikadakhala kuli zii; ngati makanda osaona kuunika.


Chinkana munthu akabala ana makumi khumi, nakhala ndi moyo zaka zambiri, masiku a zaka zake ndi kuchuluka, koma mtima wake osakhuta zabwino, ndiponso alibe maliro; nditi, Nsenye iposa ameneyo;


Thambo ndi dziko lapansi zidzachoka, koma mau anga sadzachoka ai.


ndipo mbale wolemera anyadire pamene atsitsidwa, pakuti adzapita monga duwa la udzu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa