Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 27:8 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake munda umenewu anautcha, Munda-wa-mwazi, kufikira lero lino.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake munda umenewu anautcha, Munda-wa-mwazi, kufikira lero lino.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nchifukwa chake mpaka lero mundawo umatchedwa “Munda wa Magazi.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndi chifukwa chake umatchedwa munda wamagazi mpaka lero lino.

Onani mutuwo



Mateyu 27:8
7 Mawu Ofanana  

Ndipo zinatalikitsa mphikozo, kuti nsonga za mphiko zidaoneka kulikasa chakuno cha chipinda chamkati, koma sizinaoneke kubwalo; ndipo zili komweko mpaka lero lino.


Koma anapangana, nazigula munda wa woumba mbiya, ukhale manda a alendo.


Ndipo iwo analandira ndalamazo, nachita monga anawalangiza: ndipo mbiri iyo inabuka mwa Ayuda, kufikira lero lomwe.


ndipo chinadziwika ndi onse akukhala ku Yerusalemu; kotero kuti m'manenedwe ao kadzikoka kanatchedwa Akeledama, ndiko, kadziko ka mwazi.)


Ndipo Iye anamuika m'chigwa m'dziko la Mowabu popenyana ndi Betepeori; koma palibe munthu wakudziwa kumanda kwake kufikira lero lino.


Ndipo Yoswa anaimika miyala khumi ndi iwiri pakati pa Yordani, poimapo mapazi a ansembe akusenza likasa la chipangano; ikhala komweko kufikira lero lino.


Ndipo munthuyo anamuka ku dziko la Ahiti, namanga mzinda, nautcha dzina lake Luzi; ndilo dzina lake mpaka lero lino.