Yoswa 4:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yoswa anaimika miyala khumi ndi iwiri pakati pa Yordani, poimapo mapazi a ansembe akusenza likasa la chipangano; ikhala komweko kufikira lero lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yoswa anaimika miyala khumi ndi iwiri pakati pa Yordani, poimapo mapazi a ansembe akusenza likasa la chipangano; ikhala komweko kufikira lero lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Yoswa adaimiritsa miyala khumi ndi iŵiri imene idaali pakati pa mtsinje wa Yordani, pamalo pomwe padaaimirira ansembe onyamula Bokosi lachipangano la Chauta aja. Miyala imeneyi ikadali kumeneko mpaka lero lino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yoswa anayimika miyala khumi ndi iwiri imene inali pakati pa Yorodani pamalo pamene ansembe onyamula Bokosi la Chipangano anayimapo. Ndipo miyalayo ili pamalo pomwepo mpaka lero lino. Onani mutuwo |